
Yes Lord, You are the King of
Warriors
Jehovah Jireh
Jehovah Shalom
Ndinu ling langa
Yes, Lord, You are the God of peace
You mend the broken hearts
You heal every pain
Ndinu linga langa
Ndinu linga langa
You mend broken hearts
You heal every pain
Ndinu nokha Dada
Ndinu nokha Yahweh
HOOK
Munakwapulidwa,
coz of my sins
Munanyozedwa,
kamba ka ine
Munakwapulidwa,
coz of my sins
Munanyozedwa
VERSE 2
Chipewa chaminga chikavwalikika kumutu
kwinu Dada
Mphinjika mukanyamula kutimbika nthowa
yose
Eeee Eeee
VERSE 3
Nkhondo, nkhondo Mbuye munandimenyera
Kwatsala nkwa ine kuti ndikutsateni.
Nkhondo, nkhondoMbuyemunatimenyera
Kwatsala nkwa ine kuti nditsate m’mapazi.
Yes Lord, You are the King of
Warriors
Jehovah Jireh
Jehovah Shalom
Ndinu ling langa
Yes, Lord, You are the God of peace
You mend the broken hearts
You heal every pain
Ndinu linga langa
Ndinu linga langa
You mend broken hearts
You heal every pain
Ndinu nokha Dada
Ndinu nokha Yahweh
HOOK
Munakwapulidwa,
coz of my sins
Munanyozedwa,
kamba ka ine
Munakwapulidwa,
coz of my sins
Munanyozedwa
VERSE 2
Chipewa chaminga chikavwalikika kumutu
kwinu Dada
Mphinjika mukanyamula kutimbika nthowa
yose
Eeee Eeee
VERSE 3
Nkhondo, nkhondo Mbuye munandimenyera
Kwatsala nkwa ine kuti ndikutsateni.
Nkhondo, nkhondoMbuyemunatimenyera
Kwatsala nkwa ine kuti nditsate m’mapazi.